8,99 €
inkl. MwSt.
Sofort per Download lieferbar
payback
0 °P sammeln
  • Format: ePub

Kukhalapo kwa Mulungu n'kwamtengo wapatali!
Kukhalapo kwa Mulungu n'kofunika!
Kukhalapo kwa Mulungu n'kofunika kwambiri pa miyoyo yathu, ndipo tiyenera kulikufuna ndi mitima yathu yonse. Sititha konse, m'njira iliyonse, kuchepetsa kufunika kwa kukhalapo kwa Mulungu pa kuyenda kwathu naye. Tiyenera nthawi zonse kukhala tikulifunafuna kukhalapo kwa Mulungu.
Kukhala ndi kukhalapo kodzozedwa pamodzi nanu, n'kukhala ndi Kukhalapo Kopatulika kwa Mulungu m'moyo mwanu. Ndi pemphero langa kuti mtima wanu utsitsimuke kulakalaka kukhalapo kwa Mulungu kwamtengo wapatali pamene mukuwelenga buku lodabwitsali lolemba Dag Heward-Mills.
…mehr

  • Geräte: eReader
  • mit Kopierschutz
  • eBook Hilfe
  • Größe: 1.03MB
  • FamilySharing(5)
Produktbeschreibung
Kukhalapo kwa Mulungu n'kwamtengo wapatali!

Kukhalapo kwa Mulungu n'kofunika!

Kukhalapo kwa Mulungu n'kofunika kwambiri pa miyoyo yathu, ndipo tiyenera kulikufuna ndi mitima yathu yonse. Sititha konse, m'njira iliyonse, kuchepetsa kufunika kwa kukhalapo kwa Mulungu pa kuyenda kwathu naye. Tiyenera nthawi zonse kukhala tikulifunafuna kukhalapo kwa Mulungu.

Kukhala ndi kukhalapo kodzozedwa pamodzi nanu, n'kukhala ndi Kukhalapo Kopatulika kwa Mulungu m'moyo mwanu. Ndi pemphero langa kuti mtima wanu utsitsimuke kulakalaka kukhalapo kwa Mulungu kwamtengo wapatali pamene mukuwelenga buku lodabwitsali lolemba Dag Heward-Mills.


Dieser Download kann aus rechtlichen Gründen nur mit Rechnungsadresse in A, B, CY, CZ, D, DK, EW, E, FIN, F, GR, H, IRL, I, LT, L, LR, M, NL, PL, P, R, S, SLO, SK ausgeliefert werden.

Autorenporträt
Bishop Dag Heward-Mills is a medical doctor by profession and the founder of the United Denominations Originating from the Lighthouse Group of Churches (UD-OLGC). The UD-OLGC comprises over three thousand churches pastored by seasoned ministers, groomed and trained in-house. Bishop Dag Heward-Mills oversees this charismatic group of denominations, which operates in over 90 different countries in Africa, Asia, Europe, the Caribbean, Australia, and North and South America. With a ministry spanning over thirty years, Dag Heward-Mills has authored several books with bestsellers including 'The Art of Leadership', 'Loyalty and Disloyalty', and 'The Mega Church'. He is considered to be the largest publishing author in Africa, having had his books translated into over 52 languages with more than 40 million copies in print.